Chichewa Malankhulidwe ena

KODI YESU Ndi YANI?

Kodi mukhala odabwa kuti Yesu ndi Yani?

Simuli kutali ai ndi yankho, kapena zitsulo zomwe zingathe kumuthandizani kuti muike chikhulupiriro canu mwa Yesu Kristu.

Kodi ndi zitsulo zotani zimezi?

  • Yesu ndi Yani?

    Yesu wa ku Nazareti ndani kwa inu? Yankho yani kwa funso iyi itha kusintha moyo wanu kwa nthawi yosatha.

  • Malamulo Anai A Uzimu

    Muyambira poti?  Aka ka buku kamupatsani malumo anai a uzimu omwe angathe kumuthandizani kuti mulowe mu cibwenzi ndi Mulengi.

  •  Vidiyo Ya Yesu

    Ngati mufuna zidzindikilo zeni-zeni za Umoyo wa Yesu Kristu, onani kanema iyi pa vidiyo.

  • Moyo wa Uzimu

    Ndiciani cimene cicitika pamene mulandira Yesu mwa cikhulupiriro?  Dziwani momwe mungathe kupatila mphavu ndi mtendere mwa Yesu.

Kodi muli ndi mafunso? Kodi mufuna kudziwa zambiri? Kodi mungatiuze zina? Tiuzeni.

ONANI KANEMA

jesusbox.gif (17237 bytes)

Gulan
 Tsopano


SAITI
map
u


Home Yesu Ndi Yani? Kanema ya YESU Malamulo Anai Moyo wa Uzimu Mwayi Chuma

© 2002 Campus Crusade for Christ International | webmaster@greatcom.org

Last Updated: 16 June, 2003